Intumwa zikomeza gutanga ibimenyetso no gukora ibitangaza byinshi muri rubanda, kandi bose hamwe n'umutima umwe bagakoranira mu nsi y'Ibaraza rya Salomoni.
Ndipo mwa manja aatumwi zizindikilo ndi zozizwa zambiri zinacitidwa pa anthu; ndipo anali onse ndi mtima umodzi m'khumbi la Solomo.
Si uwo se uri ku meza ?
Kodi si iye amene ali pa tebulo?
Nta wundi wabonetse ngo agaruke gushimira Imana, atari uyu munyamahanga ?"
Kodi sanapezeke wina aliyense wobwerera kudzalemekeza Mulungu koma munthu wa mtundu wina yekhayu?"
Kuko ubuntu bw'Imana buzanira abantu bose agakiza bwabonetse.
Pakuti caonekera cisomo ca Mulungu cakupulumutsa anthu onse,
'Ariko Imana yabiduhishurije Umwuka wayo, kuko Umwuka arondora byose ndetse n'amayoberane y'Imana.
Koma kwa ife Mulungu anationetsera izi mwa Mzimu; pakuti Mzimu asanthula zonse, zakuya za Mulungu zomwe.
hagati y umuriro waka, ahōre inzigo abatamenye Imana n abatumvira ubutumwa bwiza bw Umwami wacu Yesu.
Adzalanga anthu osadziwa Mulungu ndi osamvera Uthenga Wabwino wa Ambuye wathu Yesu.
Ku munsi wa karindwi Imana irangiza imirimo yakoze: iruhuka ku munsi wa karindwi imirimo yayo yose yakoze.
Popele pansiku yaŵusisanu nasiŵili ŵaLesa ŵalisilisye imilimo yaŵo iyo ŵacitile; naŵo ŵalitusisye pansiku yaŵusisanu nasiŵili, nekuleke'milimo yaŵo yonse iyo ŵacitile.
ahubwo abonye isezerano ry Imana ntiyashidikanishwa no kutizera, ahubwo akomezwa cyane no kwizera ahimbaza Imana,
ndipo poyang'anira lonjezo la Mulungu sanagwedezeka cifukwa ca kusakhulupirira, koma analimbika m'cikhulupiriro, napatsa Mulungu ulemu,
18Simvuze mwese: abo natoye ndabazi, ariko Ibyanditswe bigomba kuzuzwa ngo 'Uwo dusangira umugati ni we wanteye umugeri' 19Mbaburiye hakiri kare bitaraba, ngira ngo umunsi ibyo byabaye muzemere ko ndi Uriho.
18 Sindinena za inu nonse; ndikudziwa ndawasankha; koma kuti cholemba chikwaniritsidwe, Iye wakudya mkate adatsamilitsa chidendene chake molimbana ndi Ine.
ariko mu mpisho kuko yatinya Abayahudi,
Misuwo yonsene idamalwa fungwa mwadidi, thangwi iwo akhachita mantha na Ayuda.
Yari "byose kuri bose."
Mulungu ankawadalitsa ndipo iye anali "zinthu zonse kwa aliyense."
Yezu ati " Mwibimubuza, kuko nta muntu ushobora gukora igitangaza mu izina ryanjye, maze ngo ahindukire amvuge nabi.
Yesu anati, "Musamuletse, palibe amene amachita chodabwitsa mʼdzina langa ndipo kenaka nanena zoyipa za Ine,
Zimaze kumera, izuba ryarazibabuye ziruma kubera ko imizi yazo itashoboraga kugera kure.
Koma dzuwa litakwera, zinawauka, ndipo popeza zinalibe mizu zinafota.
Ibumburira akanwa kayo gutuka Imana, no gutuka izina ryayo n'ihema ryayo n'ababa mu ijuru.
Ndipo chinayamba kuyankhula mawu achipongwe onyoza Mulungu, dzina lake, malo okhalamo ndi onse amene amakhala kumwamba.
kuko Imana yabumbiye hamwe abantu bose mu bugome, kugira ngo ibone uko ibabarira bose.
Pakuti Mulungu anasandutsa anthu onse a mʼndende ya kusamvera kuti Iye akaonetse chifundo kwa onse.
Umwana wanjye Yozefu aracyariho!
Yosefe mwana wanga akadali ndi moyo!
Nta wigeze azamuka ajya mu ijuru, uretse Umwana w'umuntu wamanutse aturutse mu ijuru.
Palibe munthu anakwera kumwamba, koma Iye wotsikayo kuchokera Kumwamba, ndiye Mwana wa Munthu.
Ababivuga batyo, bazarebe
Pakuti iwo akunena zotere awonetserapo kuti alikufuna kuti dziko likhale lawo.
Bityo hari abo mu ba nyuma bazaba aba mbere, hakaba n'abo mu ba mbere bazaba aba nyuma."
Ndipo onani! pali omalizira amene adzakhala oyamba, ndipo alipo oyamba amene adzakhala omaliza. "
Icyajyaga kubabera cyiza, iyaba batigeze kumenya inzira yo gukiranuka, biruta ko basubira inyuma bamaze kuyimenya, bakareka itegeko ryera bahawe.
Zikadakhala bwino kuti sakadadziwiratu njira yachilungamo kuposa kudziwa atasiyana ndi lamulo loyera lomwe adalandira.
Hariho umuntu wari ufite indwara, ayimaranye imyaka mirongo itatu n'umunani.
Iye adaona munthu ule akhali wakulamala pyaka makumatatu na pisere, Munthuyo akhagona m'khundu mwa thawale yakupambulika.
Hanyuma abwira abagaragu be ati 'Iby'ubukwe byateguwe, ariko abatumiwe ntibari babikwiye.
Kenako inauza antchito ake kuti, 'Phwando lakonzeka, koma amene adayitanidwa sanali oyenera kubwera.
" Mwebwe abarindwa n'imbaraga z'Imana kubwo kwizera, murindirwa agakiza kiteguwe kuzahishurwa mu gihe cy'imperuka.
amene musungidwa ndi mphamvu ya Mulungu mwa chikhulupiriro, kufikira chipulumutso chokonzeka kukavumbulutsidwa nthawi yotsiriza.
Ntimukiture umuntu inabi yabagiriye.
Musabwezere munthu aliyense zoyipa.
Dore hagiye kuza igihe bazavuga bati 'Hahirwa ingumba n'inda zitabyaye, n'amabere atonkeje.'
Lirani thangwi ya imwe ene na ananu; thangwi zinadzafika ntsiku zakuti anthu anadzalonga: 'Anyakutsandzaya ndi akazi adasowa ana, akazi adakhonda kubala ana na ale adakhonda kuyamwisa!'
Ese wagombye gutinya imperuka?
Kodi Muyenera Kuopa Kutha kwa Dzikoli?
16Ubu se noneho mbaye umwanzi wanyu kuko mbabwije ukuri?
16Kodi tsopano ine ndasanduka mdani wanu chifukwa ndakuwuzani choonadi?
Umwana nababatura muzaba mubatuwe by'ukuri.
Chifukwa chake ngati Mwana adzakuyesani inu aufulu, mudzakhala mfulu ndithu.
mwebwe abarindwa n imbaraga z Imana ku bwo kwizera, murindirwa agakiza kiteguwe kuzahishurwa mu gihe cy imperuka.
amene musungidwa ndi mphamvu ya Mulungu mwa chikhulupiriro, kufikira chipulumutso chokonzeka kukavumbulutsidwa nthawi yotsiriza.
Ni cyo gituma dukwiriye kurushaho kugira umwete wo kwita ku byo twumvise, kugira ngo tudatembanwa tukabivamo.
1Nʼchifukwa chake, ife tiyenera kusamalira kwambiri zimene tinamva, kuopa kuti pangʼono ndi pangʼono tingazitaye.
Abenshi mu bababonye bagenda barabamenya, nuko baza ku maguru baturuka mu migi yose bahirukira, ndetse barahabatanga.
33Koma ambiri amene anawaona akuchoka anawazindikira ndipo anathamanga wapansi kuchokera mʼmidzi yonse nakayambirira kufika.
Hanyuma agarutse, asanga nanone basinziriye, kuko amaso yabo yari aremerewe; nuko ntibabona icyo bamusubiza.
40 Ndipo anadzanso nawapeza ali m'tulo, pakuti maso awo adalemeradi; ndipo sadadziwe chomuyankha Iye.
Koko rero Izayi yaravuze ati "Nyagasani, ni nde wemeye inyigisho zacu?"
Pakuti Yesaya anena, Ambuye , ndani adakhulupirira zonena zathu?
kandi nahamagaye umwana wanjye ngo ave mu Misiri.
ndipo ndinayitana mwana wanga kuti atuluke mu Igupto.
Nuko amaze kuzamurwa n'ukuboko kw'iburyo kw'Imana, no guhabwa na Se ibyo yasezeranije ari byo Mwuka Wera, none asutse icyo mureba kandi mwumva.
Khristu anakwezedwa kukhala kudzanja lamanja la Mulungu, nalandira Mzimu Woyera amene Atate anamulonjeza, ndipo watipatsa ife zimene mukuona ndi kumvazi.
None se bishoboka bite ko bavuga mu ndimi zacu?"
Ndiyeno zikutheka bwanji kuti azilankhula zilankhulo zathu?'
Anyaze abakomeye intebe zabo, Ashyize hejuru aboroheje.
Adatsitsa olamulira kuchokera pamipando yawo koma adakweza anthu onyozeka.
Mbese uragira ngo ndeke kunywa igikombe cy'umubabaro Data yampaye?"
Kodi Ine ndisamwere chikho chimene Atate andipatsa?"
ni cyo gituma ku bwanjye nshaka kubabwira ubutumwa bwiza namwe abari i Roma.
Pa chifukwa chimenechi, ine ndikufunitsitsa kulalikira Uthenga Wabwino kwa inunso amene muli ku Roma.
Ariko bene Data, sinshaka ko mutamenya yuko kenshi nagambiriraga kuza iwanyu, ngo mbone imbuto muri mwe namwe nko mu yandi mahanga, ariko ngira ibisībya kugeza na n'ubu.
Ndipo sindifuna kuti inu, abale, mudzakhala osadziwa, kuti kawiri kawiri ndikanena mumtima kuti ndikafike kwa inu, koma ndaletsedwa kufikira lero, kuti ndikaone zobala zina mwa inunso, monga mwa anthu amitundu ena.
Hanyuma abwira abagaragu be, ati 'Iby'ubukwe byateguwe, ariko abatumiwe ntibari babikwiye.
Kenako inauza antchito ake kuti, 'Phwando lakonzeka, koma amene adayitanidwa sanali oyenera kubwera.
Bibiliya igira iti "[Andereya] yabanje kujya kureba umuvandimwe we Simoni, aramubwira ati 'twabonye Mesiya' (bisobanurwa ngo Kristo)."
Baibulo limati: "Choyamba [Andireya] anapeza m'bale wake Simoni, ndi kumuuza kuti: 'Ifetu tapeza Mesiya' (dzina lotanthauza, Khristu polimasulira)."
Muririnde rero, kugira ngo mudapfusha ubusa imbuto z'ibikorwa byanyu, ahubwo ngo muzahabwe igihembo cyuzuye.
Chenjerani nokha, kuti musataye zomwe tidayesetsa kupanga, koma kuti mulandire mphotho yathunthu.
Ntitwakwemererwa kugira abagore bizera, ngo tujyane na bo, NK'UKO IZINDI NTUMWA ZIGENZA, na bene se b'Umwami Yesu na Kefa?
Kodi tiribe ufulu wotenga mkazi wachikhristu paulendo wathu, monga amachitira atumwi ena aja, kuphatikiza abale a Ambuye ndi Kefa?
Dore icyo Imana ibashakaho: ni uko mwaba intungane, mukirinda ubusambanyi.
Pakuti ichi ndichifuniro cha Mulungu, chiyeretso chanu: kuti mudzipatule chiwerewere; kuti aliyense wa inu kudziwa kulamulira thupi lake m'chiyero ndi ulemu, osati mu chilakolako cha chilakolako monga amitundu osadziwa Mulungu.
mwebwe abarindwa n imbaraga z Imana ku bwo kwizera, murindirwa agakiza kiteguwe kuzahishurwa mu gihe cy imperuka.
amene musungidwa ndi mphamvu ya Mulungu mwa cikhulupiriro, kufikira cipulumutso cokonzeka kukabvumbulutsidwa nthawi yotsiriza.
41Nuko abantu benshi cyane baremera, babitewe n'ibyo yababwiraga.
41 Pontho, na thangwi ya fala yace, azinji anango antawira.
Yezu arongera ati "Iby'Ingoma y'Imana twabigereranya n'iki, cyangwa se twabivuga mu wuhe mugani?
Ndipo ananena, Tidzafaniziranji Ufumu wa Mulungu? kapena tidzaulinganiza ndi fanizo lotani?
None, mu mugi wa Dawudi, mwavukishije Umukiza ari we Kristu Nyagasani.
Lero abalwa mpulumusi wanu mu nzinda wa Dhavidhi, ndiye Kristu Mbuya.
Icyajyaga kubabera cyiza, iyaba batigeze bamenya inzira yo gukiranuka,biruta ko basubira inyuma bamaze kuyimenya, bakareka itegeko ryera bahawe.
Zikadakhala bwino kuti sakadadziwiratu njira yachilungamo kuposa kudziwa atasiyana ndi lamulo loyera lomwe adalandira.