Ndikukupemphererani kuti mudziwe chikondi chija cha Khristu chopitirira nzeru za anthu, kuti mudzazidwe kwathunthu ndi moyo wa Mulungu mwini.
nokulwazi uthando lukaKristu oludlula ukwazi konke, ukuze nigcwaliswe kube ngukugcwala konke kukaNkulunkulu.


Ena mwa anthu anu adzapulumuka, iwo amene alembedwa m'buku.
Abanye abantu bakho bazophunyuka, labo ababhalwe phansi encwadini.

Ndimakonda Japan, kotero kuti ndakhala ndikupita kutchuthi atatu atatu apitawa.
Ngiyayithanda iJapan, kangangoba ngiye eholidini kulezi ezintathu zokugcina.

Kaya ankaganiza zotani, kuganizira malangizo amene Mulungu anamupatsa kukanamuthandiza.
Kungakhathaliseki ukuthi wayecabangani, wayengakhumbula isiyalo sikaNkulunkulu.

Komanso, dzanja la Yehova linali nawo, ndipo ambiri anakhulupirira natembenukira kwa Ambuye.
Ngaphezu kwalokho, isandla sikaJehova sasinabo, futhi inani elikhulu laba ngamakholwa laphendukela eNkosini.

Ambiri mwa atumiki a moto Mulungu.
Iningi umlilo izigqili kuNkulunkulu.

(Gen. 5:2) Pa nthawi yake yoyenerera, Mulungu adzawononga angelo oipawa.
(Gen. 5:2) Iingilozi ezimbi nezingalalelikwezi zizokutjhatjalaliswa ngesikhathi esibekwe nguZimu.

Ndikuganiza kuti inali Facebook.
Ngicabanga ukuthi bekuyi-Facebook.

Ngati anazunza ine, inunso adzakuzunzani."
Uma beye bashushisa mina, bayonishushisa nani."

Mfumukazi ya Indies ndi Mgonjetsi - Kuyambira Meyi 16
INdlovukazi yama-Indies kanye noMnqobi - Kusukela ngoMeyi 16

Munganene kuti: "Ndinapeza lemba lolimbikitsa kwambiri ili."
Ungase uthi: "Uyazi ngithole nanku umbhalo okhuthazayo."

Nthaŵi zina anali kufuna kukhala payekha polankhula ndi Mulungu.
Ngezinye izikhathi wayethanda ukuba yedwa lapho ekhuluma noNkulunkulu.

Kodi muli ndi abwenzi angati pa Facebook?.
Unabangane abangaki ku-Facebook?.

Munthu wolungama Elihu anati: "N'kutali ndi Mulungu kuchita choipa, ndi Wamphamvuyonse kuchita chosalungama."
U-Elihu othembekile wathi: "Makube kude noNkulunkulu weqiniso ukwenza ngendlela yokukhohlakala, noMninimandla onke ukwenza ngokungabi nabulungisa!"

Inu muli nawo mawu a moyo wosatha."
Nguwe onamezwi wokuphila okungapheliko."

Kwa zaka 17 ndinkapemphera kuti ndipeze mayankho a mafunso anga.
Ngathandaza iminyaka engu-17 ukuze ngithole izimpendulo zemibuzo yami.

Ndipo ndili nanu pakhungu langa.
Futhi nginawe esikhunjeni sami.

Ngakhale anthu amene amapita kutchalitchi sadziwa bwinobwino Malemba.
Ngisho nabaningi abathi bayasonta banolwazi oluncane lwemiBhalo.

Kodi mtumwi Paulo ankatanthauza chiyani ponena kuti: "Pamene ndili wofooka, m'pamene ndimakhala wamphamvu"?
Umphostoli uPawulu wayesho ukuthi lapho ebhala ukuthi: "Lapho ngibuthakathaka, kulapho-ke nginamandla"?

Chifukwa ndimakukondani, ndikufuna kukuwonetsani zomwe ndikuchita mdziko lapansi lero.
Ngoba ngiyakuthanda, ngifuna ukukukhombisa engikwenzayo emhlabeni namuhla.

iwo anaona ophunzira ake akudya chakudya ndi mʼmanja mwakuda kapena kuti mʼmanja mosasamba.
Sebebonile ukuthi abanye babafundi bakhe badla izinkwa ngezandla ezimbi okungukuthi ezingahlanjiwe -

Koma munthu akayenda usiku, amapunthwa pa chinachake chifukwa mwa iye mulibe kuwala."
Kodwa uma umuntu ehamba ebusuku, uyakhubeka, ngoba ukukhanya akukho kuye."

Ndimagwirizana ndi inu kuti Mulungu 100% zabwino.
Ngivumelana nawe ukuthi uNkulunkulu 100% okuhle.

20 Kodi tingakhale tani na cikhulupiro ninga ca Djobi?
20 Indlela esingaluhlakulela ngayo ukholo olufana nolukaJobe.

Lero ndi tsiku loyamba la moyo wanu wonse, Calvin.
Namhlanje usuku lokuqala of the impilo yakho yonke, Calvin.

Ndipo nenani kwa Arkipo, Samaliratu utumiki umene udaulandira mwa Ambuye, kuti uukwanitse.
Nimtshele u-Arkiphu, nithi: "Qaphela inkonzo oyitholile eNkosini, ukuze uyifeze."

Ukatumikira milungu yawo, umenewo udzakhala msampha kwa iwe."+
Uma kwenzeka ukhonza onkulunkulu babo, kuyoba ugibe kuwe."+

amene kale sanakupindulira, koma tsopano watipindulira bwino iwe ndi ine;
okade engenalusizo kuwe, kepha kalokhu unosizo nakuwe nakimi,

Pakuti aliyense wokhala ngati wamng'ono pakati pa nonsenu ndi amene ali wamkulu."
Ngoba lowo oziphatha njengomncane phakathi kwenu nonke nguye omkhulu."

Zimenezi nʼzofanizira chabe, ndipo zinkalozera nthawi ino, kusonyeza kuti mphatso ndi nsembe zimene zinkaperekedwa sizinkachotsa chikumbumtima cha wopembedzayo.
elona lingumfanekiso kulesi sikhathi samanje, okulethwa ngawo iminikelo nemihlatshelo engenakumenza okhonzayo aphelele maqondana nonembeza,

Ngati anazunza ine, adzakuzunzani inunso."
Uma beye bashushisa mina, bayonishushisa nani."

Izi ndi zimene mayi wina wa ku Japan ankachita pophunzitsa ana ake awiri.
Kunomma weJapan owakwenzako lokho.

Pakuti Iye amene Mulungu anamtuma alankhula mau a Mulungu; pakuti sapatsa Mzimu ndi muyeso.
Ngokuba lowo uNkulunkulu amthumileyo ukhuluma amazwi kaNkulunkulu; ngokuba akaniki uMoya ngokulinganisela.

Kodi ndani amene analenga zinthu zimenezo? . . .
Ngubani odale lezi zinto? . . .

Iye adzalanga amene sadziwa Mulungu ndi amene samvera Uthenga Wabwino wa Ambuye athu Yesu.
elangabini lomlilo, ephindisela kwabangamazi uNkulunkulu nakwabangalaleli ivangeli leNkosi yethu uJesu,

Uwalamule kuti azichita zabwino, kuti azikhala olemera pa ntchito zabwino, owolowamanja ndi okonda kugawana zinthu zawo ndi anzawo.
Bayale benze okuhle, banothe ngemisebenzi emihle; baphane babele abanye.

Ngati munthu ali yense afuna kucita cifuniro cace, adzazindikira za ciphunzitsoco, ngati cicokera kwa Mulungu, kapena ndilankhula zocokera kwa Ine ndekha.
Nanyana ngubani ofisa ukwenza intando yakhe, uzokwazi ukuthi engikufundisako kuvela kuZimu namkha ngikhuluma okuvela kimi."

Yesu anayankha nati kwa iwo, Ndinacita nchito imodzi, ndipo muzizwa monse,
UJesu waphendula wathi kubo: Ngenze umsebenzi owodwa, njalo lonke liyamangala.

Mose sanachite mantha ndi zimene Farao angachite atamva zimenezi.
UMose wayengesabi.

"Futukulani mtima wanu." - 2 Akor.
"Zivuleni ngokupheleleyo izinhliziyo zenu." - 2 Khor.

Mbuzi kaya iweyo, maina aja adatulutsidwa aja iweyo sudayaone?
Abahlambalazi igama elihle enibizwa ngalo na?

• Kodi ena afeŵetsa zinthu m'moyo wawo m'mbali ziti?
• Yiziphi izici abanye abaye benza ukuphila kwabo kwaba lula kuzo?

Komabe iye ankalambiranso Mulungu limodzi ndi banja lake.
Kodwa wayebuye amkhulekele nomndeni wakhe.

Kenako ananena kuti: "Ntchitoyi si ya munthu."
Waphinda wathi: "Lo akusimsebenzi womuntu."

Yesu anayankha kuti, "Nthawi yafika yakuti Mwana wa Munthu alemekezedwe.
UJesu waphendula, wathi kubo: "Sesifikile isikhathi sokuba ikhazimuliswe iNdodana yomuntu.

Ngati masabata angapo apitawa tidayankhula za Hong Kong ndi ...
Uma emasontweni ambalwa edlule sikhulume ngeHong Kong kanye ne ...

Pa nthawi imeneyo ambiri adzasiya chikhulupiriro ndipo adzadana ndi kuperekana wina ndi mnzake,
Njalo ngalesosikhathi abanengi bazakhubeka, banikelane, bazondane.

(Miyambo 16:24) Muziwapempha kuti akupatseni malangizo ena amene angakuthandizeni kuti muzilera bwino anawo ndipo muziwathokoza akakupatsani malangizowo.
(IzAga 16:24) Cela iseluleko sakhe futhi umbonge lapho ekunika.

Paulo anali kudziŵa chifukwa chake anthu anali kumuzunza
UPawulu wayeqonda ukuthi kungani ayeshushiswa

Monga bambo ake adachitira, David Moyes nayenso anamutcha mwana wake (David Moyes Jnr).
Njengoba nje ubaba wakhe enza, uDavid Moyes naye wabiza indodana yakhe (uDavid Moyes Jnr).