Victoria watsegulidwa lero!
UVictoria uvulelwe namhlanje!


Kwa zaka 17 ndinkapemphera kuti ndipeze mayankho a mafunso anga.
Kangangeminyaka eyi-17 bendithandaza ukuze ndifumane iimpendulo zemibuzo ebendinayo.

Komatu chikhulupiriro chinathandiza Mose kuonanso zina.
Noko ke, ukholo lukaMoses lwalungaphelelanga ekumncedeni abone ezo zinto.

Kodi mkwatibwi 'akumubweretsa' kwa "mfumu" iti, ndipo wavala bwanji?
Ngubani "ukumkani" aziswa kuye umtshakazi, ibe uvathiswe njani loo mtshakazi?

Ndipo ngati ichi chidzamveka kwa kazembe, ife tidzamgwetsa mtima, ndipo tidzakukhalitsani opanda nkhawa.
Ukuba le nto ithe yavakala kwirhuluneli, thina soyithomalalisa, ningabi naxhala nina."

Ndi zimenezi kuti ndikuweruzidwa lero ndi inu. "
Kungenxa yoku le nto ndigwetywa namhlanje nguwe. "

Chifukwa iye amawalitsira dzuwa lake pa anthu oipa ndi abwino, ndi kuvumbitsira mvula anthu olungama ndi osalungama omwe."
'Ulenza ilanga lakhe liphume kubantu abangendawo nabalungileyo nemvula uyinisa kubantu abangamalungisa nabangengomalungisa.'

Munthu amene anapatsa Aisiraeli Malamulo Khumi ochokera kwa Mulungu?
ngendoda eyanika amaSirayeli iMithetho Elishumi evela kuThixo?

Khalani inu acifundo monga Atate wanu ali wacifundo.
Yibani nesihawu, njengokuba uYihlo enesihawu.

Iye anacita zamphamvu ndi mkono wace; 6 Iye anabalalitsa odzitama ndi mlingaliro wa mtima wao,
""Wenze amandla ngengalo yakhe, Wabachithachitha abanekratshi ekucingeni kweentliziyo zabo,

Iye amadziwa chilichonse chimene munthu akuganiza ndipo amaleza mtima ndi anthu ochimwa.
Ubona yonk' into esentliziyweni yomntu yaye unomonde kubantu abonayo.

Ndipo atumwi 12 aja anali naye limodzi."
Kwaye abalishumi elinesibini babekunye naye."

"Iye anamva kupembedzera [kwa Manase] ndi pempho lake lopempha chifundo."
"Wasabela kwisibongozo [sikaManase] ibe Yena wakuva ukucela kwakhe ubabalo."

Ndipo palibe munthu adzitengera ulemuwo mwini wace, komatu iye amene aitanidwa ndi Mulungu, monga momwenso Aroni.
Kanjalo akukho mntu uzithabathela ngokwakhe imbeko leyo;oyithabathayo ngobizwe nguThixo, kwanjengoAron.

kuti cikhulupiriro canu cisakhale m'nzeru ya anthu, koma mu mphamvu ya Mulungu.
Ngoko ke ukholo lwenu malungaxhomekeki bucikweni bamntu, kodwa malusekelwe ngamandla kaThixo.

Kudzera mwa Iye aliyense amene akhulupirira, alungamitsidwa kuchoka ku tchimo lililonse limene silingachoke ndi Malamulo a Mose.
Kuye wonke umntu okholwayo ulungelelaniswa nayo yonke into ongeke ulungiswe kuyo ngumthetho kaMoses.

Ndipo pamene atenganso wobadwa woyamba kulowa naye m'dziko, anena, Ndipo amgwadire iye angelo onse a Mulungu.
Kwaye kwakhona, xa ezisa ifayile ye- izibulo saysthi, Maziqubude kuye zonke iingelosi zikaThixo.

Koma anthu a ku Nineve akanati ayambirenso makhalidwe awo oipawo, Mulungu akanawalanga.
Ukuba abantu baseNineve babenokubuyela kwiindlela zabo ezimbi, uThixo wayeza kubohlwaya.

Mwadyerera padziko, ndipo mwachita zokukondweretsani; mwadyetsa mitima yanu m'tsiku lakupha.
Nadla ubuncwane emhlabeni apha, naxhamla iziyolo, nazondla iintliziyo zenu njengamhla kuxheliweyo.

Pakuti anthu ambiri mu mzinda uno ndi ine. "
Kuba abantu abaninzi kule dolophu kunye nam. "

Nthaŵi zambiri ankapita kumeneko ndi atumwi ake.
UYesu wayesoloko ehamba nabapostile bakhe.

koma Ine ndinena kwa inu, 6 Musalumbire konse, kapena kuchula Kumwamba, cifukwa kuli cimpando ca Mulungu;
Ke mna ndithi kuni, maningakhe nifunge nento le; nokuba lizulu, ngokuba likomkhulu likaThixo;

Ndipo pamene iye anadzuka pemphero, iye anadza kwa wophunzira, nawapeza iwo ali m'tulo ndi chisoni,
wavuka ekuthandazeni, weza kubafundi bakhe, wabafumana belele ngokuba buhlungu kwentliziyo.

Posapita nthawi Aisiraeli onse anamva za chiweruzo chimenechi, ndipo anthu anazindikira kuti nzeru zimene Solomo anali nazo zinali zochokera kwa Mulungu.
Wonke uSirayeli weva ngesi sigqibo, baza abantu baqonda ukuba uSolomon unobulumko bukaThixo.

Limanenanso kuti: 'Musamanamizane.'
Kwakhona ithi: "Musani ukuxokisana."

m'mau a choonadi, mu mphamvu ya Mulungu; mwa zida za chilungamo kulamanja ndi kulamanzere,
sinelizwi lenyaniso, sinamandla kaThixo, sineentonga zobulungisa zasekunene nezasekhohlo,

Kodi zimenezi zikutanthauza kuti angelo sathandiza anthu?
Ngaba loo nto ithetha ukuba iingelosi azibancedi abantu?

Akasankha zochita mwanzeru, zinthu zingawayendere bwino.
Xa begqiba ngobulumko, bayancedakala.

"Ufumu wanga suli mbali ya dziko lino.
"Ubukumkani bam abuyonxalenye yeli hlabathi.

e khomboni ndi ḓo ima nae;
Ndiya kuba naye ndibandezelekile;

Koma kwa iwo amene anapulumutsidwa, ndiko, kuti ife, uli mphamvu ya Mulungu.
Kodwa kwabo basindisiweyo, yiyo i, kuthi, ngamandla kaThixo.

Ndipo anati, Kodi Yehova wanena ndi Mose yekha?
Bathi, UYehova uthethe ngoMoses yedwa yini na?

Ndimakonda mafunso anu!))
Ndiyayithanda imibuzo yakho!))

Izi zikutikumbutsa za abale a ku Makedoniya m'nthawi ya atumwi.
Oku kusikhumbuza abazalwana baseMakedoni benkulungwane yokuqala.

Mulungu ndi amene anatilenga m'njira yoti tizikondana.
NguThixo owasidala saba nothando.

Koma musaiwale kuti anthu amene sataya mtima ndi amene adzalandire mphoto.
Ukhumbule ke nants' into: Umvuzo uza kufunyanwa ngabo baxhathisayo.

Ndipo pomwepo ambiri adzakhumudwa, nadzaperekana wina ndi mzache.
Ngelo xesha abaninzi baya kurhoxa elukholweni, bangcatshane, bathiyane.

Koma iye anayankha, nati kwa iwo, Amai wanga ndi abale anga ndiwo amene akumva mau a Mulungu, nawacita.
Waphendula Waphendula uYesu wathi, UMama nabazalwana bam ngaba balivayo ilizwi likaThixo, balenze.

Ndipo anawawuza iwo, " ndinu ochokera pasi; ine ndi ochokera ku mwamba.
Wathi kuwo, Nina ningabangaphantsi, mna ndingowangaphezulu; Ndivela phezulu.

Phunzitsa mwana poyamba njira yace; Ndipo angakhale atakalamba sadzacokamo.
Mfundise umntwana ngendlela efanele umntwana naxa athe wamkhulu akasayi kumka kuyo.

Koma ine ndikudziwa kuti ngakhale tsopano Mulungu adzakupatsani chilichonse chimene mudzamupempha."
Kodwa nangoku ndiyazi ukuba uThixo wokunika nantoni na oyicelayo kuye. ""

kuti chikhulupiriro chanu chisatsamire pa nzeru ya anthu koma pa mphamvu za Mulungu.
Ngoko ke ukholo lwenu malungaxhomekeki bucikweni bamntu, kodwa malusekelwe ngamandla kaThixo.

Pakudulidwa oipa udzapenya."
Xa abangendawo benqunyulwa, uya kubona."

Aliyense amene waona Ine, waonanso Atate.
Lowo undibonileyo mna umbonile noBawo.

Aliyense amene amadziwa zabwino zimene amayenera kuchita koma osazichita, ndiye kuti wachimwa.
Ngoko kowaziyo ukwenza okuhle, angakwenzi, kulowo kusisono.

Kodi inu munayamba mwaganizapo Luxembourg?
Ukhe wacinga Luxembourg?

Ndipo ngati ici cidzamveka kwa kazembe, ife tidzamgwetsa mtima, ndipo tidzakukhalitsani opanda nkhawa.
Ukuba le nto ithe yavakala kwirhuluneli, thina soyithomalalisa, ningabi naxhala nina."

Kodi ndaganizira za nyengo ndi chikhalidwe cha m'dzikolo?
Ngaba ndikhe ndacinga ngemozulu nezithethe zalapho?

Ndinu kulima Mulungu; ndinu yomanga Mulungu.
Nina kulinywe kaThixo; wena nokwakhiwa kaThixo.

Yesu ananenanso kuti: "Nthawi idzafika, ndipo ndi yomwe ino, pamene olambira oona adzalambira Atate motsogoleredwa ndi mzimu ndi choonadi, pakuti Atate amafuna oterowo azimulambira."
UYesu wongeza wathi: "Liyeza ilixa, nangoku selikho, xa abanquli bokwenyaniso baya kumnqula uBawo ngomoya nenyaniso, kuba, eneneni, uBawo ufuna abanjalo ukumnqula."