Mungatowezera cikhulupiro ca Nowa, munakwanisambo kupulumusa umaso wanu na wa ale anafuna imwe.
ኣስኣሰር እምነት ኖህ እንተ ስዒብካ፡ ንስኻ እውን ንርእስኻን ነቶም እትፈትዎምን ከተድሕን ትኽእል ኢኻ።
46 Penepo, mbuya wace anadza kabwera ntsiku ikhakhonda iye kudikhira, pa n'dzidzi unakhonda iye kudziwa.
ጐይታ እቲ ባርያ እቲ፡ ንሱ ብዘይተጸበያ መዓልቲ ብዘይፈላጣ ጊዜውን ኪመጽእ እዩ።
Ndinu kulima Mulungu; ndinu yomanga Mulungu.
ንስኻትኩም ሕርሻ ኣምላኽ፡ ህንጻ ኣምላኽ ኢኹም።
64 Koma pali ena mwa inu amene sakukhulupirira."
64 ገለ ኻባኻትኩም ግና ዘይኣምኑ ኣለዉ" በሎም።
Komatu palibe ngakhale imodzi imene idzagwa pansi Atate wanu osadziwa."
ሓንቲ እኳ ኻብኣተን ብዘይ ፍቓድ ሰማያዊ ኣቦኹም ኣብ ምድሪ ኣይትወድቕን እያ።
9Iye sanasiyanitse pakati pa ife ndi iwo, pakuti anayeretsa mitima yawo mwachikhulupiriro.
9ልቦም ብእምነት ስለ ዘንጽሀ ኣብ መንጎናን ኣብ መንጎኣቶምን ሓንቲ እኳ ኣይፈላለየን።
M'malomwake ananena kuti: "Kudwala kumeneku si kwa imfa chabe, koma n'kopatsa Mulungu ulemerero, kuti mwa kudwalako, Mwana wa Mulungu alemekezeke."
የግዳስ፡ "እዚ ሕማም እዚ፡ ወዲ ኣምላኽ ብእኡ ምእንቲ ኪኸብር፡ ንኽብሪ ኣምላኽ እዩ እምበር፡ ንሞት ኣይኰነን" በለ።
Ngati nanunso mutatsanzira chikhulupiriro cha Nowa, zingathandize kuti inuyo ndi banja lanu mudzapulumuke.
ኣስኣሰር እምነት ኖህ እንተ ስዒብካ፡ ንስኻ እውን ንርእስኻን ነቶም እትፈትዎምን ከተድሕን ትኽእል ኢኻ።
Musamaope munthu aliyense, pakuti chiweruzo ndi cha Mulungu.
ፍርዲ ናይ ኣምላኽ እዩ እሞ፡ ገጽ ሰብ ኣይትፍርሁ።
Ngati nanunso mutatsanzira chikhulupiriro cha Nowa, zingathandize kuti inuyo komanso banja lanu mudzapulumuke.
ኣስኣሰር እምነት ኖህ እንተ ስዒብካ፡ ንስኻ እውን ንርእስኻን ነቶም እትፈትዎምን ከተድሕን ትኽእል ኢኻ።
Ngakhale atakuchimwirani kasanu ndi kawiri patsiku ndipo abwereranso kwa inu maulendo asanu ndi awiri nati, 'Ndalapa,' muyenera kuwakhululukira.
ኣብ መዓልቲ ሸውዓተ ሳዕ እኳ እንተ በደለካ፡ 'ተጣዒሰ' እናበለ ኸኣ ሸውዓተ ሳዕ ናባኻ እንተ ተመሊሱ፡ ሕደገሉ።
Tsopano ife tikudziwa kuti chiweruzo cha Mulungu, chotsutsa amene amachita zinthu zotere, nʼchokhazikika pa choonadi.
"ንሕናስ ኣብቶም ከምዚ ዝበለ ዚገብሩ እቲ ፍርዲ ኣምላኽ ሓቂ ምዃኑ ንፈልጥ ኢና።
35 Ndipo iye adati kwa iwo, amuna inu a Israyeli, tamachenjerani mwa inunokha za anthu awa, chimene muti muwachitire.
35 በሎም ድማ፡ኣቱም ሰብ እስራኤል፡ ኣብዞም ሰባት እዚኣቶም ክትገብርዎ እትሐስብዎ ዘሎኸም ተጠንቀቑሉ።
44 Koma iwo adaganiza kuti Iye adali m'chipilingu cha ulendo, nayenda ulendo wa tsiku limodzi; ndipo adayamba kumfunafuna Iye mwa abale awo ndi mwa anansi awo.
ምስ ሰብ መገዲ ዘሎ መሲልዎም፡ መገዲ ሓንቲ መዓልቲ ኸዱ፡ ኣብ ኣዝማዶምን ኣብ ዚፈልጥዎምን ከኣ ደለይዎ።
15Anati kwa iwo, "Pitani mʼdziko lonse lapansi ndipo mukalalikire Uthenga Wabwino kwa zolengedwa zonse.
15 ከምዚ ድማ በሎም፦ "ናብ ኵላ ዓለም ኪዱ፡ ንዅሉ ፍጥረት ከኣ ብስራት ስበኹሉ።
4 Ngakhale akuchimwire maulendo 7 pa tsiku, n'kubwera kwa iwe maulendo 7, kudzanena kuti, 'Ndalapa ine,' umukhululukire ndithu."+
ኣብ መዓልቲ ሸውዓተ ሳዕ እኳ እንተ በደለካ፡ 'ተጣዒሰ' እናበለ ኸኣ ሸውዓተ ሳዕ ናባኻ እንተ ተመሊሱ፡ ሕደገሉ።
Koma anapulumutsa Loti wolungamayo, amene anavutika mtima kwambiri ndi anthu ophwanya malamulo, mwa kulowerera kwawo khalidwe lotayirira."
ነቲ ብኣበሳኦምን ብርኹስ ንብረቶምን ዚስቀ ዝነበረ ሎጥ ጻድቕ ግና ኣድሐኖ፡
Umenewu ndi ubwino wa Allah; amaupereka kwa amene wamfuna.
ንዘደለዮ ልዕል ኣበሎ፣ ንዝደለዮ ኸኣ ኣዋረዶ።
Ngakhale atakuchimwirani kasanu ndi kawiri pa tsiku, ndikubwereranso maulendo asanu ndi awiri nkunena kuti, 'Ndalapa,' muyenera kuwakhululukira. "
ኣብ መዓልቲ ሸውዓተ ሳዕ እኳ እንተ በደለካ፡ 'ተጣዒሰ' እናበለ ኸኣ ሸውዓተ ሳዕ ናባኻ እንተ ተመሊሱ፡ ሕደገሉ።
Mpostolo Juwau adanemba kuti: 'Ule omwe an'khulupira Mwanayo ana moyo wakusaya kumala, omwe an'khulupira lini Mwanayo an'dzaugumana lini moyo, koma ukali bwa Mulungu bun'dzakhala pa iye.'
ሃዋርያ ዮሃንስ፡ "እቲ ብወዲ ዚኣምን፡ ናይ ዘለኣለም ህይወት ኣላቶ፣ እቲ ንወዲ ዘይእዘዞ ግና፡ ቍጥዓ ኣምላኽ ደኣ ኣብኡ ይነብር እምበር፡ ንህይወት ኣይኪርእያን እዩ" ኢሉ ጸሓፈ።
Kenako ananena kuti: "Choncho pitani mukaphunzitse anthu a mitundu yonse."
ሽዑ ድማ፡ 'ኪዱ ኻብ ኵሎም ኣህዛብ ደቀ መዛሙርቲ ግበሩ።
Allah ndiye Wamkulu kuposa iwo amunawo.
ኣምላኽ ካብ መዋቲ ሰብ ኣጸቢቑ ይዓቢ እዩ።
Limati: "Yehova ali pafupi ndi onse oitanira pa iye.
"የሆዋ ንዅሎም እቶም ዚጽውዕዎ፡ ንዅሎም እቶም ብሓቂ ዚጽውዕዎ ቐረባኦም እዩ።
Ngakhale anthu amene amapita kutchalitchi sadziwa bwinobwino Malemba.
መብዛሕትኦም እቶም ሃይማኖተኛታት ዚብሃሉ እውን እንተ ዀኑ፡ ብዛዕባ ቕዱሳት ጽሑፋት ሒደት ፍልጠት እዩ ዘለዎም።
January 2013 _ Kodi Muyenera Kuopa Kutha kwa Dzikoli?
ጥሪ 2013 መወዳእታ ዓለም ኬፍርሃካ ይግባእዶ፧
5 Farao anati kwa Yosefe, "Abambo ako ndi abale ako abwera kwa iwe.
5 ፈርኦን ድማ ንዮሴፍ፤ ኣቦኻን ኣሕዋትካን መጺኦምኻ።
Pakuti anthu wochimwa amachitanso chomwecho.
ከምኡስ ኃጥኣንውን ይገብሩ እዮም።
Khalani Wokhululuka 131.
ይቕረ በሃልቲ ንኹን 131.
Anapita nawo kumpoto ndi kum'mawa.
ናብ ሰሜንን ናብ ምብራቕን ተወስዱ
Popeza iwo asankha njira zawozawo,
መገድታት ርእሶም ሓርዮም፣
maso ali nawo, koma sapenya;
ኣዒንቲ ኣለዎም፡ ግናኸ ኣይርእዩን፣
Iye adzakhala wamkulu ndipo adzatchedwa Mwana wa Wammwambamwamba.
ንሱ ዓብዪ ኪኸውን፡ ወዲ እቲ ልዑል እውን ኪብሃል እዩ፣ .
Mtumwi Paulo ananenanso kuti "olungama ndi osalungama omwe" adzaukitsidwa.
ሃዋርያ ጳውሎስ እውን፡ "ንጻድቃንን ንሓጥኣንን" ትንሳኤ ኸም ዚኸውን ገሊጹ ኣሎ።
Mwina mumpingo wanu muli m'bale amene zochita kapena zolankhula zake sizimakusangalatsani.
ምናልባት ብዘረባኡን ብተግባራቱን ቅጭ ዜምጽኣልካ ሓው ኣብ ጉባኤኻ ይህሉ ይኸውን።
Komano zikugwirizana bwanji ndi nkhani yokhudza Ufumu wa Mulungu komanso chaka cha 1914?
ግናኸ እዚ ምስ መንግስቲ ኣምላኽ ኰነ ምስ 1914 እንታይ ርክብ ኣለዎ፧
14 Makolo achikhristu amafunikanso kulimba mtima.
14 ክርስትያን ወለዲ እውን ትብዓት የድልዮም እዩ።
Yesu ananenanso kuti: "Ndili ndi zambiri zakuti ndikuuzeni, koma padakali pano simungathe kuzimvetsa zonsezo."
የሱስ ቀጺሉ፡ "ገና ብዙሕ ዝነግረኩም ኣሎኒ፣ ግናኸ፡ ሕጂ ኽትጾርዎ ኣይትኽእሉን ኢኹም" በሎም።
Popeza Mulungu ndi wamuyaya, zaka 1,000 zili ngati tsiku limodzi kwa iye.
ኣምላኽ ዘለኣለማዊ ስለ ዝዀነ፡ ሽሕ ዓመት ንዕኡ ልክዕ ከም ሓንቲ መዓልቲ እዩ።
(ndikuyamba) m'dzina la Allah, kuyamikidwa konse ndi kwa Allah.
ብስም ኣላህ እቲ ፍጹም ርህሩህ እቲ ኣዝዩ ራህራሂ
Ngati mutaganizira zimene Mulungu wachitira anthu onse komanso inuyo panokha, n'zoonekeratu kuti watichitira zinthu zambirimbiri.
ብዛዕባ እቲ ኣምላኽ ንዓኻን ንደቂ ሰብ ብሓፈሻን ዝገበረልኩም ነገራት ምስ እትሓስበሉ፡ ዛጊት ብዙሕ ነገራት ከም ዝገበረ ንጹር እዩ።
Bambo anga okha ndi amene anabwerako ndi moyo.
ኣቦይ ጥራይ ከኣ እዩ ብህይወት ተሪፉ።
Iye anati: "Ndikupatsani inu lamulo latsopano, kuti mukondane wina ndi mnzake; monga ndakonda inu, kuti inunso mukondane wina ndi mnzake.
ኣስዕብ ኣቢሉ ኸኣ፡ "ንሓድሕድኩም ክትፋቐሩ፡ ከምቲ ኣነ ዘፍቀርኩኹም፡ ንስኻትኩም እውን ንሓድሕድኩም ክትፋቐሩ፡ ሓድሽ ትእዛዝ እህበኩም ኣለኹ።
Iwo ali nawo maso koma iwo sakukhoza kupenya.
ኣዒንቲ ኣለዎም፡ ግናኸ ኣይርእዩን፣
Ndimasangalala kwambiri kukhala mu utumiki tsiku lonse limodzi ndi mkazi wanga."
ምስ ሰበይተይ ምሉእ መዓልቲ ኣብ ኣገልግሎት ከሕልፎ ኸለኹ፡ ብሓቂ ዜሐጕስ እዩ" በለ።
5 Tamverani abale anga okondedwa.
5 ፍቑራት ኣሕዋተየ ስምዑ።
Mayi wina dzina lake Gail, yemwe panopa ali ndi zaka 60, anati: "Mwamuna wanga Robert, anamwalira pa 9 July, mu 2008, atachita ngozi.
"ብዓል ቤተይ ሮበርት ኣብ 9 ሓምለ 2008 እዩ ሞይቱ።
Ngakhale akuchimwire maulendo 7 pa tsiku, n'kubwera kwa iwe maulendo 7, kudzanena kuti, 'Ndalapa ine,' umukhululukire ndithu."
ኣብ መዓልቲ ሸውዓተ ሳዕ እኳ እንተ በደለካ፡ 'ተጣዒሰ' እናበለ ኸኣ ሸውዓተ ሳዕ ናባኻ እንተ ተመሊሱ፡ ሕደገሉ።
Iye ananena kuti atumwi okhulupirikawo limodzi ndi anthu ena adzalamulira ndi Yesu kumwamba.
እወ፡ እቶም እሙናት ሃዋርያትን ካልኦትን ኣብ ሰማይ ምስኡ ሓቢሮም ኪገዝኡ እዮም።
Ndithudi Allah akudziwa, pomwe inu simudziwa (chinsinsi cha zinthu.)
እና ፈለጥኩም ዘይከውን ኣይትስርሑ።
"Allah amafafaniza zimene wafuna ndi kulimbikitsa (kuti zisachoke zomwe wafuna), ndipo gwero la malamulo onse lili kwa Iye (Allah).
እቲ ጸጊሙ ዘሎ ሰብ ቦታ አምላኽ ሒዙ በቲ ንሱ ዝደልዮ ንኸምኡ ዝበለ ሰብ ክመርሕ ምድላዩ እዩ።