Naye omu ku mmwe mulyolyomi."
Komabe mmodzi wa inu ndi mdierekezi."


Kubanga, laba, ntonda eggulu eriggya n'ensi empya: so ebintu ebyasooka tebirijjukirwa so tebiriyingira mu mwoyo.
"Ndilenga kumwamba kwatsopano [boma latsopano la kumwamba] ndi dziko lapansi latsopano [mtundu wa anthu olungama watsopano] ndipo zinthu zakale sizidzakumbukika, pena kulowa mumtima.

Olwo ne balaba omwana w'omuntu ng'ajjira mu bire, ng'alina obuyinza bungi n'ekitiibwa kinene.
Kenako adzaona Mwana wa munthu akubwera mumtambo ndi mphamvu ndi ulemerero waukulu."

Olwo ne balaba omwana w'omuntu ng'ajjira mu bire, ng'alina obuyinza bungi n'ekitiibwa kinene.
Ndipo adzaona Mwana wa munthu alimkudza mu mtambo ndi mphamvu ndi ulemerero waukulu ."

Essanyu ery'emirembe n'emirembe liriba nga ngule ku mitwe gyabwe.
Ndipo wosatha chimwemwe kudzakhala pa mitu yawo.

Obujulizi bwabwe (bwe bepampalika okuwa) bujja kuwandiikibwa era bagenda kubuuzibwa.
Umboni wawo ulembedwa ndipo adzafunsidwa (pazimenezo)!

Bazadde bange tebaagenda naye nze nnagenda.
Makolo anga sanapite koma ine ndinapita.

kubanga ndabye byonna Labbaani by'akukolera.
Chifukwa ndaona zonse zimene Labani wachita kwa inu.

Tewali Katonda yakolebwa okusooka nze,
Ine ndisanakhaleko kunalibe Mulungu amene anapangidwa."

Mmutoraine kuba omuheereza wangye ow'omutaano.'
Ndam'sankha akhale mtumiki wanga wapadera.'

tuli bantu be era endiga ez'omu ddundiro lye.
Ndife anthu ake ndi nkhosa za pabusa pake."

Enkya bajja kumanya ani mulimba omwerazi.
"Mawa lino adzadziwa (tsiku lakuwatsikira chilango,) kuti ndiyani wabodza wodzitukumula (iwo kapena Swaleh).

3611:36 nny 3Awo Abayudaaya ne bagamba nti, "Ng'abadde amwagala nnyo!"
11:36 Choncho, Ayuda anati, "Onani mmene anamkonda!"

Nnyinza ntya okukuwaayo ggwe Isirayiri?
Kodi ndingakupereke bwanji iwe Israeli?

abaweereza bange bajja kunywa,
atumiki anga adzamwa,

Ekikompe Kitange ky'ampadde, siikinywe?"
Kodi Ine ndisamwere chikho chimene Atate andipatsa?"

17 Ebyo Maliyamu bye yayogera.
17 Zimene Mariya ankalankhula.

Olwo nno ndyoke mbalumbire ddala nga mbava mu maaso ne mabega waabwe ne ku ddyo waabwe ne kkono, era togenda kusanga abasinga obungi mu bo nga beebaza.
"Kenako ndidzawadzera (mbali ya) kutsogolo kwawo, m'mbuyo mwawo, kumbali yakumanja kwawo ndi kumanzere kwawo, mwakuti simudzapeza ambiri a iwo oyamika.

Kyandibadde kirungi singa omuntu oyo teyazaalirwa ddala."
Zikanakhala bwino munthu ameneyu akanapanda kubadwa."

(Abantu abo) tebagenda kubeera na kya kulya kyonna okugyako e miti egy'amaggwa.
Ndipo alibe chakudya kupatula Mafinya (a anthu akumoto)

'Abatuukirivu' abanaazuukizibwa be baani?
Kodi mbani 'anyakulungama' omwe an'dzalamusidwa?

"Emirembe gibe mu ggulu, n'ekitiibwa kibeere waggulu ennyo!"
"Mtendere kumwamba ndi ulemerero mmwambamwamba!"

Ne tuzimba waggulu wa mmwe emyaliiro emigumu musanvu.
Ndipo tamanga pamwamba panu thambo Zisanu ndi ziwiri zolimba;

Mazima bombi ba mu baddu baffe abakkiriza (abannamaddala).
Ndithu, iye adali mmodzi mwa akapolo athu okhulupirira.

Muwulirize mmwe amawanga gonna,
Imvani inu anthu a mitundu yonse;

Omulumenhu oo a twikululwa okwa nyamukula a ti: "Omufimanekwa, Omona womunhu olyelye opo ndi mu itavele?"
Munthuyo anayankha kuti: "Kodi mwana wa munthuyo ndani ndimudziwe bambo, kuti ndikhulupirire mwa iye?"

Kyandibadde kirungi singa omuntu oyo teyazaalirwa ddala."
Kukanakhala bwino kwa iye akanapanda kubadwa."

Kiki nnabbi eyava mu Yuda ky'ataakola, era kiki ekyavaamu?
Kodi mneneri wa ku Yuda analephera kuchita chiyani, nanga zotsatira zake zinali zotani?

Yokaana ajja kuba nnabbi, era ajja kuteekerateekera Masiya ekkubo.'
Juwau an'dzakhala mpolofeta, ndipo iye an'dzakonzera njira Mesiya.'

17 Pi meno, medde ki lweny ki tekki ducu.
17 Tenepo pitirizani kumenya nkhondo.

Nebagamba nti tukkirizza Mukama Katonda omulabirizi w'ebitonde.
"Adati: "Takhulupirira Mbuye wa zolengedwa zonse."

"Ebintu ebingi [omuntu] by'aba nabyo si bye bimuwa obulamu."
Baibulo limanena kuti moyo wa munthu "suchokera m'zinthu zimene ali nazo."

Atanjagala, ebigambo byange tabikwata.
Amene sandikonda ine sasunga mawu anga."

n'awa abantu ebirabo."
ndipo anapereka mphatso kwa anthu."

Kale Katonda wammwe alibawonya atya mu mukono gwange?' "
Ndipo mulungu amene adzakulanditsani m'manja mwanga ndani?'

N'ayogera nti, "Abantu badduse mu lutalo, era bangi ku bo bafudde.
"Ndipo iye anati: "Anthu athawa kunkhondo, ndipo anthu ambiri agwa nafa.

"Pe dong gibimedde ki pwonyo lweny"
"Anthuwo sadzaphunziranso nkhondo"

Baba obaddeki Navio, Zamba ki temusiima?
Kodi bwanji sathokoza (Allah)?

nnaamukuumanga, kubanga amanyi erinnya lyange.
Ndidzamuteteza chifukwa wadziwa dzina langa.

Abaana baabwe balikiraba ne basanyuka,
Ana awo adzaziona zimenezi ndipo adzasangalala;

38 Weena orikuunyikiriza, emigyera y'amaizi g'amagara eryahimintika neeruga omunda ye, nk'oku Ebyahandiikirwe birikugira.
Wokhulupirira mwa ine, monga Lemba limati, kutuluka m'kati mwake idzasonkhana wa madzi amoyo.

'Nkusaba otugezese okumala ennaku 10,' bw'atyo bw'amugamba.
'Chonde tiyeseni kwa masiku 10,' akutero.

Nga mugamba nti, 'Buli akola ebintu ebibi mulungi mu maaso ga Yakuwa, era amusanyukira,'+ oba nti, 'Katonda omwenkanya ali ludda wa?'"
Mwamutopetsa ponena kuti, "Aliyense amene amachita zoyipa ndi wabwino pamaso pa Yehova ndipo iye amakondwera naye" kapena pofunsa kuti, "Ali kuti Mulungu woweruza mwachilungamo?"

2Yaabagira ati: Hakaba hariho omuramuzi omu kirorero kimwe, owaabaire atatiina Ruhanga, nobu kwakuba okweta aha muntu.
Iye anati, "Mʼmudzi wina munali woweruza wosaopa Mulungu ngakhalenso kulabadira za anthu.

Ndimuwonya era ndimuwa ekitiibwa.
ndidzamupulumutsa ndi kumulemekeza.

Emaali yaabwe n'abaana baabwe tebigenda kubagasa naakamu mumaaso g'a Katonda.
"Chuma chawo, ngakhale ana awo, sizidzawathandiza konse ku chilango cha Allah.

Nagira ati, "Omwoyo w'amazima ku ariija aryabeebembera omu mazima goona."
Koma iyeyo akadzafika, mzimu wa choonadi, adzakutsogolerani m'choonadi chonse."

Ebibala byagwo (okumanya bibi) biringa emitwe gya Sitane.
"Zipatso zake (nzoipa) ngati mitu ya asatana.

Olina emikwano gy'abasajja emeka ku facebook?
Kodi muli ndi abwenzi angati pa Facebook?.

(a) Abaruumi 8:30 egamba " era be yayawula edda, abo era yabayita: era be yayita, yabawa abo era obutuukirivu: era be yawa obutuukirivu, yabawa abo era ekitiibwa."
Rom 8:30 Ndipo amene Iye adawalamuliratuwo, Iye adawayitana ndipo iwo amene adawayitana adawalungamitsa,ndipo iwo amene adawalungamitsa adawapatsanso ulemerero.