Kulemba cha Yoze Unafupiwa Ukwaso 45.
Pemphelo ya Munthu Wovutika 45.
Jino atumine weka nawa, oloze vamujihile.
Anatumizanso ena ambiri; ena a iwo anawamenya, ena anawapha.
Echi chikiko chalingishile vatu vayoye myaka yayivulu.
Chifukwa chake, yakhala ndi moyo wautali.
Nge mwapwa muvakulwane, kaha vyuma muka navimikafwa mwijive ngwenu mutu napihilila chikupu nakwalumuka?
Ngati ndinu mkulu, kodi mungadziwe bwanji ngati munthu walapa ndi mtima wonse?
Vatu kana vapwile vamuchisemunwino chakusokesa 7 kufuma hali Alama.
Iye anali wa m'badwo wa 7 kuchokera pa Adamu.
Yosefwe naMaliya valikomokelele hakwivwa vyumevi.
Koma Mariya ndi Yosefe anadabwa kum'peza ali kumeneko.
Zangi Yenu Kanda Nayiholako
Musalole Kuti Cikondi Canu Cizilale
Shikaho weshowo mwalinyisa nge ou mwana wamundende, ikiye wamulemu muWangana wamelu.
Chifukwa chake yense amene adzichepetsa yekha monga kamwana aka, yemweyo ali wopambana mu Ufumu wa Kumwamba.
Apwile nawa navana vamalunga vatanu navavali, vamapwevo vapwile vatatu.
Mulungu mbampasa ana amuna anomwe na acikazi atatu akubalika.
"Litwaminenu kulizakaminanga hakuyoya chenu ngwenu namulya ika, chipwe hamijimba yenu ngwenu namuvwala ika. . . .
Ananena kuti: "Lekani kudera nkhawa moyo wanu kuti mudzadya chiyani kapena kudera nkhawa matupi anu kuti mudzavala chiyani. . . .
Achishinganyekenu hachihula chino, Vyuma muka vyeji kulingisanga vatu vapwenga vakuwahilila?
Taganizirani funso ili: Kodi n'chiyani chimathandiza anthu kuti azisangalala?
Vyuma Ngwasakwile Omu Ngwapwile Ngukanyike
Zimene Ndinasankha Ndili Mwana
Oloze kutala kachi vamwene vyuma kweseka namuze veji kuvimonanga vatu tahi?
Koma kodi iwo akanatha kuona zinthu mmene ife timazionera?
Kɛ bɛ muɛ gu mua mu yingi mawove, mua gu lɔ mu mu giiyei mawove kɔlongɔ mu yingi ma.
30Nʼchifukwa chake pakati panu ambiri mwa inu ndi ofowoka ndi odwala, ndipo ambirinso agona tulo.
Michima yenu kanda nayilizakamina, chipwe kulizuzukila nawomako.
Mitima yanu isavutike kapena kuchita mantha.
Ambile ngwenyi: "Kuviza kanechi kacheshi chakutwala kukufwako, oloze chinapu chakumutohweselaho Kalunga, mangana naMwanaKalunga vahase kumutohweselaho."
M'malomwake ananena kuti: "Kudwala kumeneku si kwa imfa chabe, koma n'kopatsa Mulungu ulemerero, kuti mwa kudwalako, Mwana wa Mulungu alemekezeke."
"Namukevwa jijita namijimbu yajijita.
"Mudzamva phokoso la nkhondo ndi mbiri za nkhondo.
Te masu ni ka ka'vi i ña'a ma ji'in suchi kuechi ma.
Anthu omwe amakuvutitsani nthawi zonse amayenera kuti awombedwe pamphuno.
Kaha apwilenga navana vamapwevo nawa.
Iye anali'nso ndi ana akazi.
Ngwapwile nakutwama namama navayayami vamapwevo vatatu.
Ndinkakhala ndi mayi anga komanso azichemwali anga atatu.
2 Uno vyuma muka navitulingisa tuhulise ngwetu: "Palanga nakumwaka uka?"
2 Kodi n'ciyani comwe cingaticitise kubvunza kuti 'Mpaka lini?'
Shi tuswele Leza, le tukamona kwenda ku kupwila namani?
Ngati timakonda Mulungu, kodi tiziona bwanji misonkhano?
Mandumbu a ku Tesalonika te kali kanawa!
Abale wa ku Tesalonika wakhali bwino-bwino!
Pamo mwalitwile mbandu halivoko chipwe kulipwesula mumambuli.
N'kutheka kuti munavulala dzanja kapena bondo.
37 Ngunatachikiza vene ngwami enu mwapwa muvana vaApalahama.
37 Ine ndikudziwa kuti inu ndinu zidzukulu za Abrahamu.
37 Ngunatachikiza vene ngwami enu mwapwa muvana vaApalahama.
37 Ine ndikudziwa kuti inu ndinu zidzukulu za Abrahamu.
"Mwanami Ngwazanga Muli Mwata Kaha Nawa Wakushishika"
"Mwana Wanga Wokondedwa ndi Wokhulupilika mwa Ambuye"
Omu Riana akumishile shikola, ateselemo lushiko lwenyi.
Riana atamaliza sukulu anakwaniritsa lonjezo lake.
Mumu liaka tunafupu hashi haha?
N'cifukwa ciani dziko latsopano lifunika?
Nguli jino namyaka 83, kaha nguchili lika ngukalama muchikungulwilo.
Panopa ndili ndi zaka 83 koma ndikutumikirabe monga mkulu.
Uno Mweji Kulamanga "Mangana Amwenemwene" Tahi?
Kodi 'Mumasunga Nzeru Zopindulitsa'?
7 Kanda ulikomokelako omu ngunakulweze ngwami: Enu vatu mwatela kusemuka cheka.
7 Usadabwe chifukwa ndidati kwa iwe, uyenera kubadwa mwatsopano.
Uno unakwivwa kuwaha hakwijiva ngwove kaweshi ukawoveko tahi? -
Kodi wasangalala kudziwa kuti suli wekha? -
Kalunga keshi kwongako.
Mulungu sanganame.
Uno ngwafwelela Kalunga tahi?
Kodi ndimakhulupirira Mulungu?
Kaha ceka nawa, ove ikaze weji kumulumbilixilanga ndumbwove?
Kapena iwenso upeputsiranji mbale wako?
Oloze ngana muze chapwile kushikulu, Kalunga kaha ikiye atongwelenga lwola lwakulwa jita nakusakula vaze vatelele kulwa jita kana.
Komabe mofanana ndi m'nthawi ya Aisiraeli, Mulungu ndi yemwe ankasankha woti amenye nkhondo komanso nthawi yoyenera kumenya nkhondoyo.
Kalunga amulwezele Apalahama ngwenyi kangweshi kukanongesa Sotomeko nge namukwapwa vaka-kwoloka likumi.
Koma Mulungu anamutsimikizira kuti ngakhale mu Sodomu mutapezeka anthu 10 olungama, Iye sakanawononga mzindawo.
8 Muka-tanga wapwevo apwa iya?
8 Kodi mbewu ya mkaziyo ndi ndani?
Chizechene ngwe apostolo, ni yetwe nawa twakwambujola sango jipema ku zuwo ni zuwo.
Mofanana ndi atumwi, timalalikila nyumba ndi nyumba.
Okwo kuli vavali chipwe vatatu navakungulukila muliji na lyami, ami nangupwanga navo hamwe."
Pakuti kumene kuli awiri kapena atatu asonkhanira m'dzina langa, ndiri komweko pakati pao.
KAPETULU 69 Uno Sevo Apwile Apalahama Nyi Liyavolo?
MUTU 69 Kodi Atate Wawo Anali Abulahamu Kapena Mdyerekezi?
Kwamba chake ni chake ila chenu ni cha wote.
Ulamuliro (wazinthu zonse) uli kwa Iye ndipo kwa Iye ndi kumene mudzabwerera nonsenu.
Mwomwo Kalunga kaveshi kumweseka navyuma vyavipiko, kaha ikiye nawa keshi kweseka mutu naumweko.
Pakuti Mulungu sangayesedwe ndi zinthu zoipa ndipo iye sayesa munthu ndi zinthu zoipa.
Zangi yavatu vavavulu nayikahola mwomwo yakuvula chaupapwoki."
Anthu ambiri adzakhala osamvera malamulo ndipo chikondi cha anthu ambiri chidzazirala.
Kaha lichako ngwawanyine uze mukulwane walizavu ali ukawenyi.
Tsiku lotsatila, n'nakumana ndi mtsogoleli wa gulu limenelo ali yekha.
Nyi te kasakwile kwononokena Zambi, kachi katwama miaka yeswe mu Paraisu hano hashi.
Iwo akanamvera Mulungu, akanakhala ndi moyo wosatha m'Paradaiso padziko lapansi.
Kamba Mukreste ukona kuhapelezwa ki bahabo yena kuli anyale kamba kunyalwa asika supala kale.
Mbale yomwe ili ndi chakudya cha kamba iyenera kukhala yoyera;
KAPITULU 6 Mutu Nyi Hafwa Kulihi Akuya?
MUTU 6 Kodi Munthu Akafa Amapita Kuti?
Tunatange chino: "Ivwenu chiseke, yenu malilu, ni yenu nwatwamamo!"
Timawerenga kuti: "Kondwerani kumwamba inu ndi inu okhala kumeneko!"