Kakuli coko ya ka i bubebe, mi mulwalo wa ka ha u na bukiti."
Pakuti goli langa ndi losavuta ndipo katundu wanga ndi wopepuka."
Natani alilabiile ati: "Kamucita fyonse ifili mu mutima wenu; pakuti baLesa bali nenu."
Natani anati: "Chitani chilichonse chimene chili mumtima mwanu, chifukwa Mulungu woona ali nanu."
Kabili Sekaria pakumona alisakamikwe, no mwenso walimwikete.
Ndipo Zekariya anadabwa pamene anamuona, ndipo mantha anamgwira.
Lelo nshilemona ifyo fileampana na 1914.
Komabe sindikuona kugwirizana kwa zimenezi ndi chaka cha 1914.
Bushe ali no kuupa umwanakashi na umbi?
Kodi iye adzakwatira mkazi wina?
"Tata untabukile bukata" (28)
"Baba ndi nkulu kupiringana ine" (28)
Cisuma ukukwata abanobe abengi."
Zimakhala bwino kukhala ndi anzako ambiri."
5Pantu Lesa alishiba ukuti ilyo mukalyako, amenso yenu yakesuka elyo mukaba nga Lesa, mukeshiba ifisuma ne fibi."
5Pakuti Mulungu akudziwa kuti tsiku lomwelo la YANU kudya zipatso zake YANU maso adzatseguka ndipo inu adzakhala ngati Mulungu, WODZIWA zabwino ndi zoipa. "
Myaka 12 pa kupita'po, twetana nandi monka mu New York.
Patapita zaka 12, tinakumananso ku New York.
Ifipande fyaba muli Loleni! ifitila "Abacaice Bepusha Ukuti"
Nkhani za mu Galamukani! zakuti, "Zimene Achinyamata Amadzifunsa"
October 2015 _ Amepusho Yatatu ayo Abantu Bengatemwa Ukwipusha Lesa
October 2015 _ Mafunso Atatu Omwe Anthu Amafuna Atafunsa Mulungu
Yesu alefwaya ukubapeela umulimo.
Yesu anali ndi ntchito yoti awapatse.
"Kashā Kekwaikele Muntu Unena Nabya"
"Nthaŵi Yonse Palibe Munthu Analankhula Chotero"
Jon: Bwisambila pa bulopwe.
Jon: Lembali lanenanso za ufumu.
Nansha le wiivwananga na mweivwanine Ed?
Kapena mumamvela monga mmene Ed anamvelela?
Mu bipangwa byonso bya Leza, mikōko yādi imweka bu isakilwa bukwashi kutabuka, enka na ayo yāpangilwe mwanda wa kwikale muntu wa kwiyendeja ne kwiilama.
Pa zolengedwa zonse, nkhosa zinkaoneka kuti sizingayende zokha koma zinkafunika munthu woti azizitsogolera komanso kuziteteza.
Bushe Kwaliba Uwingeshiba Ifya ku Ntanshi?
Kodi Pali Amene Angadziwiretu za M'tsogolo?
Inya, panuma ya kufumyapo ukubifya konse ne bantu imbifi pa calo.
Inde, atachotsera dziko kuipa konse ndi anthu oipa.
Kabili Sekaria pakumona alisakamikwe, no mwenso walimwikete.
Ndipo Zakariya anadabwa pamene anamuona, ndipo mantha anamgwira.
Nga kanshi nashuka shani ica kuti nyina wa kwa Shikulu ese kuli ine?
Zatheka bwanji kuti mayi wa Mbuye wanga abwere kwa ine?
Kani abantu abengi balabona shani imilimo bapyunga?
Kodi anthu ambiri amaona bwanji ntchito yawo?
Kabalabila ati: "Mukabeshibila ku fisepo fyabo."
Iye anati: "Mudzawazindikira ndi zipatso zawo."
Bushe Kwaliba Uwingeshiba Ifya ku Ntanshi?
Kodi Pali Amene Angadziwiretu Zam'tsogolo?
Ico cipusho calyaswikwe mu 1931.
Funso limeneli linayankhidwa m'chaka cha 1931.
E ico bamwipwishe abati: "Itempele ili lyakuulilwe mu myaka 46, bushe iwe ukalimya mu nshiku shitatu?"
Pamenepo Ayuda anati, Kachisi uyu anamangidwa zaka 46, ndipo kodi inu mudzamuutsa masiku atatu?
Kupwa, twesonga mu Kenya.
Kenako tinakwatirana ku Kenya.
Umu 1980 yatutumile uku Nigeria.
Mu 1980 tinatumizidwa ku Nigeria.
Abebele ati: 'Mwikafuma mu Yerusalemu.
Anawauza kuti: 'Musachoke mu Yerusalemu.
Paaleni Ukulongana Kwesu 94.
Dalitsani Misonkhano Yathu 94.
Le Tufwaninwe Kutyina Satana?
Kodi Satana Tizimuopa?
3 Naashi tave shi mu ningile, osheshi inava shiiva Tate, vo kave shii nge.
3Iwo adzachita zoterozo chifukwa sanadziwe Atate kapena Inenso.
Lelo ici cacitike pa kuti twi-icetekela fwe bene, lelo tucetekele Lesa uubuusha abafwa.
Zinatero kuti tisakhale ndi chikhulupiriro mwa ife tokha, koma mwa Mulungu amene amaukitsa akufa.
Ukulongana kwa muputule ukwa kubalilapo uko twasangilweko mu El Salvador
Msonkhano wathu woyamba ku El Salvador
E lyo abepwishe ati: "Bushe uyu umutwe ne fi balembapo fya kwa nani?"
Ndiyeno anawafunsa kuti: "Kodi nkhope iyi ndi mawu akewa n'zandani?"
I vyani vino kasema umwi wino atalumbulwa uwafumile ku Yuda wafizilwe ukucita, nupya icani cafumilemo?
Kodi n'kuphonya kuponi komwe mpolofeta wa ku Juda adacita, ndipo n'ciyani comwe cidadzacitika?
Ee, naliimwena no kushininkisha ukuti, uyu e Mwana wakwa Lesa."
Penepo ine ndaona, pontho ndisacita umboni kuti uyu ndiyedi Mwana wa Mulungu."
Awe, na Yobo wine te fyo atontonkenye.
Ayi, ndipo nayenso Yobu sanaganize choncho.
Lyene Mose uumile umu ciliwe imiku iili, na manzi aingi yatandika ukufuma.
Ndiyeno Mose akumenya thanthwe'lo kawiri ndi ndodo, ndipo madzi ochuluka anatulukamo.
(Pantu ifi fyonse e fyo Abena fyalo bafwaya).
Pakuti anthu a mitundu ina akufunafuna mwakhama zinthu zonsezi.
Kabili ici e cishibilo muleishibilako: Mulesanga akanya nabakapomba mu nsalu kabili nakalaala mu ca kuliilamo ifitekwa."
Ndipo ichi ndi chizindikiro kwa inu: mudzapeza mwana wakhanda wokuta ndi nsalu atagona modyera.
10 Inte cine cine balasakamana abantu.
10 Mboni zimasamaladi anthu.
Mulefwaya Ubufumu, Mwilafwaya Ifyuma
Muzifunafuna Ufumu Osati Zinthu Zina
Bamama abafyele bamayo basambilile icine mu 1908.
Mayi awo a mayi angawa anaphunzira choonadi mu 1908.
Lelo, bafwile 'ukulaikala ifi fine na bakashi babo ukulingana no kwishiba.'
M'malomwake ayenera 'kupitiriza kukhala ndi akazi awo mowadziwa bwino [kapena kuti mowaganizira ndi kuwamvetsa].'
(Ku ca kumwenako, bushe ulomfwana bwino na bantu bambi?
(Mwachitsanzo, kodi mumacheza bwino ndi anthu?
(Ku ca kumwenako, bushe ulomfwana bwino na bantu bambi?
(Mwachitsanzo, kodi mumacheza bwino ndi anthu?
Nalyasukile ati, "Nshishibilepo uuli onse uwikala ku China."
Ndinamuuza kuti: "Sindidziwa munthu aliyense ku China."
Bamwaswike abati: 'Twalitiinine!
Iwo anayankha kuti: 'Timaopa.
Bushe Mulakwata "Ifya Kulya pa Nshita Yalinga"?
Kodi Mukulandira "Chakudya pa Nthawi Yoyenera?"
Wa nsansa umuntunse uucita ifi."
Wodala ndi munthu amene amachita zimenezi."