ከእውነቱ መንገድም ታገዱ።
njira yanji akuchotsedwa ku (choonadi)!
" 'ቤቴ ለሕዝቦች ሁሉ የጸሎት ቤት ይባላል' ተብሎ አልተጻፈምን?
Podzudzula olakwawo, iye akuti: "Sichilembedwa kodi, Nyumba yanga idzatchedwa nyumba yakupempheramo anthu a mitundu yonse?
አስታዉስም: አንተ አስታዋሽ ብቻ ነህና።
"Basi, kumbutsa (anthu) ndithu iwe, ndiwe mkumbutsi.
የአምላክን ቃል የሚወዱ ሰዎች ይህን እውነታ የተገነዘቡት ከረጅም ጊዜ በፊት ነው።
Anthu okonda Mawu a Mulungu anazindikira mfundo imeneyi kalekale.
ብሉ፤ ጥቂትንም ጊዜ ተጠቀሙ፤ እናንተ አመጠኞች ናችሁና።
"Idyani, sangalalani pang'ono m'kanthawi kochepa; ndithu inu ndinu ochimwa (chifukwa chakumphatikiza Allah ndi zolengedwa).
አለበለዚያ እንደ እሳት የዮሴፍን ቤት ያወድማል፤
mukapanda kutero Iye adzatentha nyumba ya Yosefe ngati moto;
አላህ ሰባትን ሰማያት አንዱ ካንዱ በላይ ሲኾን እንዴት እንደፈጠረ አታዩምን?
"Kodi simudaone momwe Allah adalengera thambo zisanu ndi ziwiri mosanjikizana?
ይህም እነዚያን የበደሉትን ሊያስፈራራ በዐረብኛ ቋንቋ ሲኾን (የፊቶቹን መጻሕፍት) አረጋጋጭ መጽሐፍ ነው።
Ndipo buku ili likuikira umboni (za bukulo) m'chiyankhulo cha Chiarabu kuti liwachenjeze amene adzichitira okha chinyengo, ndi kuti likhale uthenga wabwino kwa ochita zabwino.
ሆኖም እነዚህ ሰዎች በቅዱሳን መጻሕፍትና በአምላክ መንፈስ እርዳታ ለውጥ ማድረግ ችለዋል።
Iwo anasintha chifukwa chothandizidwa ndi Malemba komanso mzimu woyera wa Mulungu.
የእግዚአብሔር ጠላት ነው የሚሆነው።
Iye adzakhala nyamalwa wa Mulungu.
ባሎች, ሚስቶቻችሁን ውደዱ, በእነሱም ላይ መራራ አትሁን.
Inu amuna, musaleke kukonda akazi anu ndipo musamawapsere mtima kwambiri.
የቅዱስ ቁርኣን የመጀመሪያው አንቀጽ ‹‹አንብብ በዚያ (ሁሉን) በፈጠረው ጌታህ ስም።
(Iwe, Mneneri (SAW), zomwe Zikuvumbulutsidwa) Mdzina la Mbuye Wako yemwe adalenga (zolengedwa Zonse).
ወይም የረኃብ ባለቤት በሆነ ቀን ማብላት፤
Kapena kuwadyetsa (osowa) pa Masiku a njala
] ታላቁ የቁጣዉ ቀን መጥቶአልና፤ ማንስ ሊቆም ይችላል?
Pakuti mkwiyo wake tsiku lalikulu wabwera, ndipo amene angaime?
ጥር 2013 _ የዓለም መጨረሻ ሊያስፈራህ ይገባል?
January 2013 _ Kodi Muyenera Kuopa Kutha kwa Dzikoli?
ከአሥር ወንዶች ልጆች እኔ አልበልጥብሽም?
Kodi si ine woposa ana amene ukufunawo?'
ሙሴ "ዛሬ ሕይወትንና በረከትን፣ ሞትንና ጥፋትን በፊትህ አኑሬአለሁ" በማለት ተናግሮ ነበር።
Mose ananena kuti: "Ndaika pamaso panu lerolino moyo ndi zokoma, imfa ndi zoipa."
ከጻድቃንም ጋር አይጻፉ።
ndipo asalembedwe pamodzi ndi olungama.
ኀያልም በኀይሉ አይመካ፤
wamphamvu asadzitamandire m'mphamvu yache,
የጻድቃን ቀንድ ግን ከፍ ከፍ ይላል።
koma nyanga za olungama zidzakwezedwa.
"ከአላህ ሌላ ሲኾኑ ይረዱዋችኋልን ወይስ ለራሳቸው ይርረዳሉን"
Kodi angathe kukuthandizani kapena kudzithandiza okha?"
ከምድር ምንን እንደ #ፈጠሩ# አሳዩኝ ወይም በሰማያት ለእነርሱ መጋራት አላቸውን?
Tandionetsani, ndimbali iti ya nthaka adalenga; kapena iwo ali ndi gawo m'thambo; (gawo lakulenga thambo?)
ሆኖም እሱ ለመረጣቸው ምርጦች ሲል ቀኖቹን አሳጥሯል።
Koma chifukwa cha osankhidwawo amene anawasankha, wafupikitsa masikuwo. "
እጠይቃለሁ ፣ "እነሱ አሁንም በ NFL ውስጥ ናቸው?
Ndikufunsa, "Kodi akadali mu NFL?."
"ከእናንተ ጥበበኛና አስተዋይ ማን ነው?
"Kodi wanzeru ndi womvetsa zinthu ndani pakati pa inu?
ቅኖች በማለዳ ይገዟቸዋል፤
Olungama adzawalamulira mmawa;
ጌታችሁም " ብታመሰግኑ በእርግጥ እጨምርላችኋለሁ ብትክዱም (እቀጣችኋለሁ) ቅጣቴ በእርግጥ ብርቱ ነውና " በማለት ባስታወቀ ጊዜ (አስታውሱ) ፡ ፡
"Ndipo (kumbukani) pamene Mbuye wanu adalengeza kuti: "Ngati muthokoza, ndikuonjezerani; ndipo ngati simuthokoza (dziwani kuti) chilango changa nchaukali."
ላባ በአንተ ላይ የሚያደርገውን ሁሉ አይቼአለሁና።
Chifukwa ndaona zonse zimene Labani wachita kwa inu.
የምንሰማ ወይንም የምናስብ በነበርን ኖሮ በነዳጅ እሳት ጓዶች ውስጥ ባልሆን ነበር ይላሉ።
Ndipo adzanena: "Tikadakhala kuti Tidamvera (zimene ankatiuza) kapena Kuziganizira mwanzeru sitikadakhala M'gulu la anthu akumoto.
"ወንድና ሴትን ፈጥሯቸዋል ፤ እርሱም ባረካቸው ፣ በተፈጠሩበት ቀን በአዳም ስም ጠራቸው "።
"Adalenga iwo mwamuna ndi mkazi; ndipo anawadalitsa, nawatcha dzina la Adamu, tsiku lomwe anawalengedwa. "
እርሱንም ቤተሰቦቹንም በጠቅላላ አዳንናቸው ፡ ፡
" (Kumbuka) pamene tidampulumutsa iye ndi anthu ake onse.
የሚሰብኩት መልእክትና የሚሰብኩበት ምክንያት
uthenga umene amalalikira komanso chifukwa chake amalalikira?
የሚሰብኩት መልእክትና የሚሰብኩበት ምክንያት
uthenga umene amalalikira komanso chifukwa chake amalalikira?
5፥35 እንዲህም አላቸው፦ የእስራኤል ሰዎች ሆይ፥ ስለ እነዚህ ሰዎች ምን እንደምታደርጉ ለራሳችሁ ተጠንቀቁ።
Act 5:35 Ndipo iye adati kwa iwo, amuna inu a Israyeli, tamachenjerani mwa inunokha za anthu awa, chimene muti muwachitire.
12_22_ጥንካሬውንም በደረሰ ጊዜ ጥበብንና ዕውቀትን ሰጠነው።
"Ndipo (Mûsa) pamene adakula nsinkhu wake ndi kulingana bwino tidampatsa nzeru ndi maphunziro.
ወንድም ፒርስን በጣም እንደምንናፍቀው የታወቀ ነው።
N'zoona kuti tidzamusowa M'bale Pierce.
"እነዚያንም የሚጋደሉዋችሁን (ከሓዲዎች) በአላህ መንገድ ተጋደሉ።
"Ndipo menyanani nao nkhondo pa njira ya Allah (modziteteza) amene akukuthirani nkhondo.
የኖኅን ሦስት ወንዶች ልጆች ስም ታውቃለህ?
Kodi mukudziwa mayina atatu a ana a Nowa?
" በእውነት አበሰርንህ ፡ ፡ ከተሰፋ ቆራጮችም አትኹን " አሉ ፡ ፡
"Iwo adati: "Takuuza nkhani yabwinoyi mwachoonadi; choncho, usakhale mwa otaya mtima."
ስለ ሳይንስ ያለህ እውቀት በአምላክ ማመን አስቸጋሪ እንዲሆንብህ አድርጓል?
Kodi zimene munkadziwa zokhudza sayansi zinapangitsa kuti muvutike kuyamba kukhulupirira Mulungu?
እነዚያንም በአላህ መንገድ ላይ የተገደሉትን ሥራዎቻቸውን ፈጽሞ አያጠፋባቸውም።
Ndipo amene aphedwa panjira ya Allah, ntchito yawo sadzaipititsa pachabe.
4የከተማውም ሕዝብ ተከፋፈለ፤ ገሚሱ ከአይሁድ ጋር፣ ገሚሱም ከሐዋርያት ጋር ሆነ።
4Anthu a mu mzindamo anagawikana; ena anali mbali ya Ayuda, ena mbali ya atumwi.
ከሚደጋገሙ የኾኑን ሰባትንና ታላቁንም ቁርኣን በሙሉ በእርግጥ ሰጠንህ።
"Ndipo ndithu takupatsa (Ayah izi) zisanu ndi ziwiri zomawerenga kawirikawiri, (Sûrat Al-Fatihah), ndi Qur'an yolemekezeka.
እግዚአብሔር ሕዝቡን ፍጹም ለማድረግ ሕግን አልሰጠም ለማድረግ (ትክክለኛ እና ቅዱስ) ።
Mulungu sanapereke lamulo kuti anthu ake akhale angwiro (olungama ndi oyera).
23|35|"እናንተ በሞታችሁና ዐፈርና አጥንቶችም በኾናችሁ ጊዜ እናንተ (ከመቃብር) ትወጣላችሁ በማለት ያስፈራራችኋልን
"Kodi akukulonjezani kuti mukadzafa ndikusanduka dothi ndi mafupa, mudzaukitsidwanso (m'manda)?
ከበላያችሁ ሰባትን ብርቱዎች (ሰማያት) ገነባን።
Ndipo tamanga pamwamba panu thambo Zisanu ndi ziwiri zolimba;
"ከኛ መካከል በእርሱ ላይ (ብቻ) ማስገንዘቢያ (ራእይ) ተጣለለትን?
"Kodi am'vumbulutsira iye chikumbutso pakati pathu, (pomwe tili nawo oposa iye pa ulemelero)?
መላእክቱና መንፈሱም ልኩ አምሳ ሺሕ ዓመት በኾነ ቀን ውስጥ ወደእርሱ ያርጋሉ፤ (ይወጣሉ) ።
"Angelo ndi Jiburil amakwera kwa Iye (Allah) m'tsiku lomwe kutalika kwake kuli ngati zaka zikwi makumi asanu (50 000).
ማንኛችንም ብንሆን አምላክን አይተን አሊያም አንድ ነገር ሲፈጠር ተመልክተን አናውቅም።
N'zoona kuti palibe munthu amene anaonapo Mulungu kapena kuona zinthu zikulengedwa.
አቤቱ ጌታችን, ምን ያምር ሁሉ ስምህ በምድር ነው!
Vesi 1: O Ambuye, Ambuye wathu, dzina lanu ndi labwino bwanji padziko lonse lapansi!